1 Mafumu 22:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu ya Israyeli inati kwa Yehosafati, Alipo munthu wina kuti tifunsire kwa Yehova mwa iye; koma ndimuda, popeza samanenera za ine zabwino, koma zoipa; ndiye Mikaya mwana wace wa Yimla. Nati Yehosafati, Isamatero mfumu.

1 Mafumu 22

1 Mafumu 22:2-15