1 Mafumu 20:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu ya Israyeli anaitana akulu onse a dziko, nati, Tazindikirani inu, penyani kuti-munthu uyu akhumba coipa; popeza anatuma kwa ine kulanda akazi anga, ndi ana anga, ndi siliva, ndi golidi wanga; ndipo sindinamkaniza.

1 Mafumu 20

1 Mafumu 20:5-17