1 Mafumu 2:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati iye, Mudziwa kuti ufumu unali wanga, ndi kuti Aisrayeli onse anaika maso ao pa ine, kuti ndikhale mfumu ndine; koma ufumu watembenuka nukhala wa mbale wanga, popeza iye anaulandira kwa Mulungu.

1 Mafumu 2

1 Mafumu 2:11-18