1 Mafumu 2:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pakuyandikira masiku ace a Davide akuti amwalire, analamulira Solomo mwana wace, nati,

2. Ndimuka ine njira ya dziko lonse: limba mtima tsono, nudzionetse umunthu;

1 Mafumu 2