1 Mafumu 19:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati, Ine ndinacitira cangu Yehova Mulungu wa makamu; popeza ana a Israyeli anasiya cipangano canu, napasula maguwa anu a nsembe, napha aneneri anu ndi lupanga, ndipo ndatsala ndekha, ndipo afuna moyo wanga kuucotsa.

1 Mafumu 19

1 Mafumu 19:5-19