1 Mafumu 15:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Basa mwana wa Akiya, wa nyumba ya Isakara, anampangira ciwembu; ndipo Basa anamkanthira ku Gibetoni wa Afilisti, popeza Nadabu ndi Aisrayeli onse adamangira misasa Gibetoni.

1 Mafumu 15

1 Mafumu 15:24-34