1 Mafumu 15:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakhale pangano pakati pa ine ndi inu, pakati pa atate wanga ndi atate wanu; taonani, ndatumiza kwa inu mphatso ya siliva ndi golidi, tiyeni lilekeke pangano liri pakati pa inu ndi Basa mfumu ya Israyeli, kuti andicokere.

1 Mafumu 15

1 Mafumu 15:15-21