1 Mafumu 1:51 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu anakauza Solomo, kuti, Taonani, Adoniya aopa mfumu Solomo, popeza taonani, wagwira nyanga za guwa la nsembe, nati, Mfumu Solomo alumbirire ine lero kuti sadzandipha kapolo wace ndi lupanga.

1 Mafumu 1

1 Mafumu 1:46-53