1 Mafumu 1:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Natani ananena ndi Batiseba amace wa Solomo, nati, Kodi sunamva kuti Adoniya mwana wa Hagiti walowa ufumu, ndipo Davide mbuye wathu sadziwa?

1 Mafumu 1

1 Mafumu 1:1-14