1 Atesalonika 2:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ife, abale, angakhale adaticotsa kusiyana nanu kanthawi, osapenyana maso, koma kusiyana mtima ai, tinayesetsa koposa kuona nkhope yanu ndi cilakolako cacikuru;

1 Atesalonika 2

1 Atesalonika 2:10-18