1 Akorinto 7:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti mwamuna wosakhulupirayo ayeretsedwa mwa mkaziyo, ndi mkazi wosakhulupira ayeretsedwa mwa mbaleyo; ngati sikukadatero, ana anu akadakhala osakonzeka, koma tsopano akhala oyera.

1 Akorinto 7

1 Akorinto 7:7-16