1 Akorinto 6:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kapena kodi simudziwa kuti oyera mtima adzaweruza dziko lapansi? Ndipo ngati dziko lapansi liweruzidwa ndi inu, muli osayenera kodi kuweruza timilandu tocepacepa?

1 Akorinto 6

1 Akorinto 6:1-4