1 Akorinto 4:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tiri opusa ife cifukwa ca Kristu, koma muli ocenjera inu mwa Kristu; tiri ife ofoka, koma inu amphamvu; inu ndinu olemekezeka, koma ife ndife onyozeka.

1 Akorinto 4

1 Akorinto 4:9-17