1 Akorinto 3:4-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Pakuti pamene wina anena, ine ndine wa Paulo; koma mnzace, Ndine wa Apolo; simuli anthu kodi?

5. Ndipo Apolo nciani, ndi Paulo nciani? Atumiki amene munakhulupirira mwa iwo, yense monga Ambuye anampatsa.

6. Ndinanka ine, anathirira Apolo; kama Mulungu anakulitsa.

1 Akorinto 3