1 Akorinto 3:19-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

19. Pakuti nzeru ya dziko ina lapansi iri yopusa kwa Mulungu, Pakuti, kwalembedwa, iye agwira mzeru m'cenjerero lao;

20. ndiponso Ambuye azindikira zolingirira za mzeru, kuti ziri zopanda pace.

21. Cifukwa cace palibemmodzi adziamande mwa anthu. Pakuti zinthu onse nzanu;

1 Akorinto 3