1 Akorinto 14:35-40 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. Koma ngati afuna kuphunzirakanthu afunseamuna ao aiwo okha kwao; pakuti kunyazitsa mkazi kulankhula mu Mpingo.

36. Kodi mau a Mulungu anatutuka kwa iw? kapena anafika kwa inu nokha?

37. Ngatiwinaayesa kuti ali mneneri, kapena wauzimu; azindikire kuti zimene ndilemba kwa inu ziri lamulo la Ambuye,

38. Koma ngati wina akhale wosadziwa, akhale wosadziwa.

39. Cifukwa cace; abale anga, funitsitsani kunenera, ndipo musaletse kulankhula malilime.

40. Koma zonse zicitike koyenera ndi kolongosoka.

1 Akorinto 14