1 Akorinto 13:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti tsopano tipenya m'kalirole, ngati cimbuuzi; koma R pomwepo maso ndi maso. Tsopano ndizindikira mderamdera; koma pomwepo ndidzazindikiratu, monganso ndazindikiridwa.

1 Akorinto 13

1 Akorinto 13:4-13