17. Ngati thupi lonse likadakhala diso, kukadakhala kuti kununkhiza?
18. Koma tsopano, Mulungu anaika ziwalo zonsezo m'thupi, monga anafuna.
19. Koma ngati zonse zikadakhala ciwalo cimodzi, likadakhala kuti thupi?
20. Kama tsopano pali ziwalo zambiri, kama thupi limodzi.
21. Ndipo dise silingathe kunena kwa dzanja, Sindikufuna iwe, kapenanso mutu kwa mapazi, Sindikufunani inu.